Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Yohane 3:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

iye wocita cimo ali wocokera mwa mdierekezi, cifukwa mdierekezi amacimwa kuyambira paciyambi. Kukacita ici Mwana wa Mulungu adaonekera, ndiko kuti akaononge nchito za mdierekezi,

Werengani mutu wathunthu 1 Yohane 3

Onani 1 Yohane 3:8 nkhani