Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Yohane 3:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

osati monga Kaini anali wocokera mwa woipayo, namupha mbale wace. Ndipo anamupha iye cifukwa ninji? Popeza nchiro zace zinali zoipa, ndi za mbaie wace zolungama.

Werengani mutu wathunthu 1 Yohane 3

Onani 1 Yohane 3:12 nkhani