Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Timoteo 6:19-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. nadzikundikire okha maziko okoma ku nyengo ikudzayi, kuti akagwire moyo weni weniwo.

20. Timoteo iwe, dikira cokusungitsa, ndi kulewa zokamba zopanda pace ndi zotsutsana za ici cichedwa cizindikiritso konama;

21. cimene ena pocibvomereza 1 adalakwa ndi kutaya cikhulupiriro. Cisomo cikhale nanu.

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 6