Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Timoteo 6:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

amene iye yekha ali nao moyo wosatha, wakukhala m'kuunika kosakhozeka kufikako; amene munthu sanamuona, kapena sakhoza kumuona; kwa iye kukhale ulemu ndi mphamvu yosatha. Amen.

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 6

Onani 1 Timoteo 6:16 nkhani