Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Timoteo 5:5-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Koma iye amene ali wamasiye ndithu, nasiyidwa yekha, ayembekezera Mulungu, nakhalabe m'mapembedzo ndi mapemphero usiku ndi usana.

6. Koma iye wakutsata zomkondweretsa, adafa pokhala ali ndi moyo,

7. Ndipo izi ulamulire, kuti akhale opanda ciremao

8. Koma ngati wina sadzisungiratu mbumba yace ya iye yekha, makamaka iwo a m'banja lace, wakana cikhulupiriro iye, ndipo aipa koposa wosakhulupira.

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 5