Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Timoteo 3:2-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Ndipo kuyenera woyang'anira akhale wopanda cirema, mwamuna wa mkazi mmodzi, wodzisunga, wodziletsa, wolongosoka, wokonda kucereza alendo, wokhoza kuphunzitsa;

3. wosati woledzera, kapena womenyana ndeu; komatu wofatsa, wopanda ndeu, wosakhumba cuma;

4. woweruza bwino nyumba yace ya iye yekha, wakukhala nao ana ace omvera iye ndi kulemekezeka konse.

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 3