Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Petro 5:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mulungu wa cisomo conse, amene adakuitanani kulowa ulemerero wace wosatha mwa Kristu, mutamva zowawa kanthawi, adzafikitsa inu opanda cirema mwini wace, adzakhazikitsa, adzalimbikitsa inu.

Werengani mutu wathunthu 1 Petro 5

Onani 1 Petro 5:10 nkhani