Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Petro 4:17-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Cifukwa yafika nthawi kuti ciweruziro ciyambe pa nyumba ya Mulungu; komangati ciyamba ndi ife, citsiriziro ca iwo osamvera Uthenga Wabwino wa Mulungu cidzakhala ciani?

18. Ndipo ngati munthu wolungama apulumuka ndi kuyesetsa kokha kokha, munthu wosapembedza ndi wocimwa adzaoneka kuti?

19. Koteronso iwo akumva zowawa monga mwa cifuniro ca Mulungu aike moyo wao ndi kucita zokoma m'manja a Wolenga wokhulupirika.

Werengani mutu wathunthu 1 Petro 4