Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Petro 1:21-25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. cifukwa ca inu amene mwa rye mukhulupirira Mulungu 4 wakwnuukitsa iye kwa akufa, ndi kumpatsa iye ulemerero; kotero kuti cikhulupiriro canu ndi ciyembekezo canu cikhale pa Mulungu.

22. Popeza 5 mwayeretsa moyo wanu pakumvera coonadi kuti 6 mukakonde abale ndi cikondi cosanyenga, mukondane kweni kweni kucokera kumtima;

23. 7 inu amene mudabadwanso, osati ndi mbeu yofeka, komatu yosaola, mwa mau a Mulungu amoyo ndi okhalitsa.

24. Popeza,8 Anthu onse akunga udzu,Ndi ulemerero waowonse ngad duwa la udzu.Udzuwo ungotota, ndi duwa lace lingogwa;

25. 9 Koma Mau a Mulungu akhala cikhalire.Ndipo 10 mau olalikidwa kwa Inu ndi jawo.

Werengani mutu wathunthu 1 Petro 1