Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Atesalonika 5:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Koma za nthawizo ndi nyengozo, abale, sikufunika kuti tidzakulemberani,

2. Pakuti inu nokha mudziwa bwino kuti tsiku la Ambuye lidzadza monga mbala usiku,

3. Pamene angonena, Mtendere ndi mosatekeseka, pamenepo cionongeko cobukapo cidzawagwera, monga zowawa mkazi wa pakati; ndipo sadzapulumuka konse.

4. Kama inu, abale, simuli mumdima, kuti tsikulo likakugwereni monga mbala;

Werengani mutu wathunthu 1 Atesalonika 5