Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Atesalonika 3:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Cifukwa cace, posakhoza kulekereranso, tidabvomereza mtima atisiye tokhaku Atene;

2. ndipo tinatuma Timoteo, mbale wathuyo ndi mtumiki wa Mulungu m'Uthenga Wabwino wa Kristu, kuti akhazikitse inu; ndi kutonthoza inu za cikhulupiriro canu;

3. kuti asasunthike wina ndi zisautso izi, pakuti mudziwa nokha kuti adatiika ife ticite izi.

4. Pakutinso, pamenetinali ndi inu tinakuuziranitu kuti tidzamva zisautso; monga kudacitika, monganso mudziwa.

5. Mwa ici inenso, posalekereranso, ndinatuma kukazindikira cikhulupiriro canu, kuti kaperta: woyesa akadakuyesani, ndipo cibvuto cathu cikadakhala copanda pace.

Werengani mutu wathunthu 1 Atesalonika 3