Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 3:19-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Pakuti nzeru ya dziko ina lapansi iri yopusa kwa Mulungu, Pakuti, kwalembedwa, iye agwira mzeru m'cenjerero lao;

20. ndiponso Ambuye azindikira zolingirira za mzeru, kuti ziri zopanda pace.

21. Cifukwa cace palibemmodzi adziamande mwa anthu. Pakuti zinthu onse nzanu;

22. ngati Paulo, kapena Apolo, kapena Kefa, kapena dziko apansi, kapena moyo, kapena imfa, capena za makono ano, kapena drinkudza; zonse ndi zanu;

23. kona inu ndinu a Kristu; ndi Kristu ndiye wa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 3