Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 3:16-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Kodi simudziwa kuti muli Kacisi wa Mulungu, ndi kuti Mzimu wa Mulungu agonera mwa inu?

17. Ngati wina aononga kacisi wa Mulungu, ameneyo Mulungu adzamuononga; pakuti kacisi wa Mulungu ali wopatulika, ameneyo ndi inu.

18. Munthu asadzinyenge yekha; igati winaayesa kuti ali wanzeru nwa inu m'nthawi yino ya pansi iano, akhale wopusa, kuti akakhale vanzeru.

19. Pakuti nzeru ya dziko ina lapansi iri yopusa kwa Mulungu, Pakuti, kwalembedwa, iye agwira mzeru m'cenjerero lao;

20. ndiponso Ambuye azindikira zolingirira za mzeru, kuti ziri zopanda pace.

21. Cifukwa cace palibemmodzi adziamande mwa anthu. Pakuti zinthu onse nzanu;

22. ngati Paulo, kapena Apolo, kapena Kefa, kapena dziko apansi, kapena moyo, kapena imfa, capena za makono ano, kapena drinkudza; zonse ndi zanu;

23. kona inu ndinu a Kristu; ndi Kristu ndiye wa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 3