Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 2:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndani wa anthu adziwa za munthu, koma mzimu wa munthuyu uli mwa iye? momwemonso za Mulungu palibe wina azidziwa, koma Mzimu wa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 2

Onani 1 Akorinto 2:11 nkhani