Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 16:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Koma za copereka ca kwa oyera mtima, mongandinalangiza Mipingo ya ku Galatiya, motero citani inunso.

2. Tsiku loyamba la sabata yense wa inu asunge yekha; monga momwe anapindula, kuti zopereka zisacitike pakudza ine.

3. Ndipo pamene ndifika, ndidzatuma iwo amene mudzawayesa oyenera, ndi akalata, apite nayo mphatso yanu ku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 16