Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 15:48-52 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

48. 14 Monga wanthakayo, ateronso anthaka; ndi monga wakumwamba, ateronso akumwamba.

49. Ndipo 15 monga tabvaia fanizo la wanthakayo, tidzabvalanso fanizo la wakumwambayo.

50. Koma ndinena ici, abale, kuti 16 thupi ndi mwazi sizingathe kulowa Ufumu wa Mulungu; kapena cibvundi sicilowa cisabvundi.

51. Taonani, ndikuuzani cinsinsi; 17 sitidzagona tonse, koma tonse tidzasandulika,

52. m'kamphindi, m'kutwanima kwa diso, pa lipenga lotsiriza; pakuti 18 lipenga lidzalira, ndipo akufa adzaukitsidwa osabvunda, ndipoife tidzasandulika.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 15