Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 14:11-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Cifukwa cace, ngati sindidziwa mphamvu ya mauwo ndidzakhala kwa iye wolankhulayo wakunja, ndipo wolankhulayo adzakhala wakunja kwaine.

12. Momwemo inunso, popeza muli ofunits its a mphatso zauzimu, funani kuti mukacuruke kukumangirira kwa Mpingo,

13. Cifukwa cace wolankhula lilime, apemphere kuti amasule.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 14