Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 14:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Tsatani cikondi; koma funitsitsani mphatsozauzimu, koma koposa kuti mukanenere.

2. Pakuti iye wakulankhula lilime salankhula ndi anthu, koma ndi Mulungu; pakuti palibemunthu akumva; koma mumzimu alankhula zinsinsi.

3. Koma iye wakunenera alankhula ndi anthu comangirira ndi colimbikitsa, ndi cosangalatsa,

4. Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 14