Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 12:25-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

25. koma kuti ziwalo zifanane ndi kusamalana cinandicinzace,

26. Ndipocingakhale ciwalo cimodzi cimva cowawa, ziwalo zonse zimva pamodzi; cingakhale cimodzi cilemekezedwa, ziwalo zonse zikondwera naco pamodzi,

27. Koma inundinu thupi la Kristu, ndi ziwalo, yense pa yekha.

28. Ndipotu Mulunguanailea ena m'Eklesia, poyamba arumwi, aciwiri aneneri, acitatu aphunzitsi, pamenepo zozizwa, pomwepo mphatso zamaciritso, mathandizo, maweruziro, malilime a mitundu mitundu.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 12