Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 11:9-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. pakutinso mwamuna sanalengedwa cifukwa ca mkazi;

10. koma mkazi cifukwa ca mwamuna; cifukwa ca ici mkazi ayenera kukhala nao ulamuliro pamutu pace, cifukwa ca angelo.

11. Komanso mkazi sakhala wopanda mwamuna, kapena mwamuna wopanda mkazi, mwa Ambuye.

12. Pakuti monga mkazi aliwa kwa mwamuna, comweconso mwamuna ali mwa mkazi; koma zinthu zonse ziri za kwa Mu, lungu.

13. Lingirirani mwa inu nokha: Kodi nkuyenera kuti apemphere kwa Mulungu, wosapfunda mutu?

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 11