Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 10:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Sicinakugwerani inu ciyeso koma ca umunthu; koma Mulungu ali wokhulupirika, amene sadzalola inu kuyesedwa koposa kumene mukhoza; koma pamodzi ndi ciyeso adzaikanso populumukirapo, kuti mudzakhoze kupirirako.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 10

Onani 1 Akorinto 10:13 nkhani