29. 6 kuti thupi liri lonse lisadzitamande pamaso pa Mulungu.
30. Koma kwa iye muli inu mwa Kristu Yesu, 7 amene anayesedwa kwa ife nzeru ya kwa Mulungu, ndi cilungamo ndi ciyeretso ndi ciombolo;
31. kuti monga mwalembedwa, iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye.