Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 7:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nena kwa anthu onse a m'dziko, ndi kwa ansembe, kuti, Muja mukasala ndi kulira mwezi wacisanu, ndi wacisanu ndi citatu, zaka izi makumi asanu ndi awiri, kodi mukasalira Ine, Inedi?

Werengani mutu wathunthu Zekariya 7

Onani Zekariya 7:5 nkhani