Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 1:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsiku la makumi awiri ndi cinai la mwezi wakhumi ndi cimodzi, ndiwo mwezi wa Segati, caka caciwiri ca Dariyo, mau a Yehova anadza kwa Zekariya mwana wa Berekiya, mwana wa Ido mneneri, ndi kuti,

Werengani mutu wathunthu Zekariya 1

Onani Zekariya 1:7 nkhani