Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 1:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinati kwa mthenga wakulankhula ndi ine, Izi nziani? Ndipo anandiyankha, Izi ndi nyangazi zinabalalitsa Yuda, Israyeli, ndi Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 1

Onani Zekariya 1:19 nkhani