Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoweli 3:19-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Aigupto adzasanduka bwinja, ndi Edomu adzasanduka cipululu copanda kanthu, cifukwa ca ciwawaci anawacitira ana a Yuda; popeza anakhetsa mwazi wosacimwa m'dziko lao.

20. Koma Yuda adzakhala cikhalire, ndi Yerusalemu ku mibadwo mibadwo.

21. Ndipo ndidzayeretsa mwazi wao umene sindinauyeretsa, pakuti Yehova akhala m'Ziyoni.

Werengani mutu wathunthu Yoweli 3