Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoweli 2:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Pamaso pao mitundu ya anthu ikumva zowawa, nkhope zonse zitumbuluka.

7. Athamanga ngati amphamvu; akwera linga ngati anthu a nkhondo; niliyenda liri lonse njira yace, osasokonezeka m'mabande ao.

8. Sakankhana, ayenda liri lonse m'mopita mwace; akagwa m'zida, siityoka nkhondo yao.

9. Alumphira mudzi, athamanga palinga, akwerera nyumba, alowera pamazenera ngati mkhungu.

Werengani mutu wathunthu Yoweli 2