Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 9:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa iye, Akapolo anu afumira dziko la kutalitali, cifukwa lea dzina la Yehova Mulungu wanu; pakuti tidamva mbiri yace, ndi zonse anacita m'Aigupto,

Werengani mutu wathunthu Yoswa 9

Onani Yoswa 9:9 nkhani