Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 9:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamyankha Yoswa nati, Popeza anatiuzitsa akapolo anu kuti Yehova Mulungu wanu analamulira mtumiki wace Mose kukupatsani dziko lonseli, ndi kupasula nzika zonse za m'dziko pamaso panu; potero tinaopera kwambiri moyo wathu pamaso panu, ndipo tinacita cinthuci.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 9

Onani Yoswa 9:24 nkhani