Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 9:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Yoswa anyengedwa ndi Agibeoni napangana nao. Ndipo kunali, pakumva ici mafumu onse a tsidya ilo la Yordano, kumapiri ndi kucidikha, ndi ku madoko onse a nyanja yaikuru, pandunji pa Lebano: Ahiti ndi Aamori, Akanani, Aperizi, Ahivi, ndi Ayebusi;

2. anasonkhana kuponyana ndi Yoswa ndi Israyeli, ndi mtima umodzi.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 9