Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 7:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yoswa, ndi Aisrayeli onse naye, anatenga Akani mwana wa Zera, ndi siliva, ndi marayawo, ndi cikute cagolidi, ndi ana ace amuna ndi akazi, ndi ng'ombe zace, ndi aburu ace, ndi nkhosa zace, ndi hema wace ndi zace zonse; nakwera nazo ku cigwa ca Akori.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 7

Onani Yoswa 7:24 nkhani