Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 6:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mudziwo udzaperekedwa kwa Yehova ndi kuonongeka konse, uwu ndi zonse ziri m'mwemo; Rahabi yekha wadamayo adzakhala ndi moyo, iye ndi onse ali naye m'nyumba, cifukwa anabisa mithenga tinawatumawo.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 6

Onani Yoswa 6:17 nkhani