Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 3:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Yoswa, Ndi ici mudzadziwa kuti Mulungu wamoyo ali pakati pa inu, ndi kuti adzapitikitsa ndithu pamaso panu Akanani, ndi Ahiti, ndi Ahivi, ndi Aperizi, ndi Agirigasi, ndi Aamori, ndi Ayebusi.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 3

Onani Yoswa 3:10 nkhani