Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 24:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yoswa anati kwa anthu onse, Taonani, mwala uwu udzakhala mboni yotitsutsa; pakuti udamva mau onse a Yehova amene ananena kwa ife; ndipo udzakhala mboni yotsutsa inu, mungakanize Mulungu wanu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 24

Onani Yoswa 24:27 nkhani