Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 24:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ngati kutumikira Yehova kukuipirani mudzisankhire lero amene mudzamtumikira, kapena milungu imene anaitumikira makolo anu okhala tsidya lija la mtsinje, kapena milungu ya Aamori amene mukhala m'dziko lao; koma ine, ndi a m'nyumba yanga, tidzatumikira Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 24

Onani Yoswa 24:15 nkhani