Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 21:17-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Ndipo motapira pfuko La Benjamini, Gibeoni ndi mabusa ace, Geba ndi mabusa ace,

18. Anatotu ndi mabusa ace, ndi Alimoni ndi mabusa ace; midzi inai.

19. Miclzi yonse ya ana a Aroni, ansembe, ndiyo khumi ndi itatu, ndi mabusa ao.

20. Ndipo mabanja a ana a Kohati, Aleviwo, otsala a ana a Kohati, analandira midzi ya maere ao motapira pa pfuko la Efraimu.

21. Ndipo anawapatsa Sekemu ndi mabusa ace ku mapiri a Efraimu, ndiwo mudzi wopulumukirako wakupha mnzaceyo, ndi Gezeri ndi mabusa ace;

22. ndi Kibizaimu ndi mabusa ace, Betihoroni ndi mabusa ace; midzi inai.

23. Ndipo motapira m'pfuko La Dani, Eliteke ndi mabusa ace, Gibetoni ndi mabusa ace;

24. Aijaloni ndi mabusa ace, Gati-rimoni ndi mabusa ace; midzi inai.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 21