Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 21:11-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Ndipo anawapatsa mudzi wa Ariba, ndiye atate wa Anoki, womwewo ndi Hebroni, ku mapiri a Yuda, ndi mabusa ace ozungulirapo.

12. Koma minda ya mudzi ndi miraga yace anapatsa Kalebe mwana wa Yefune, ikhale yace.

13. Ndipo kwa ana a Aroni wansembe anapatsa Hebroni ndi mabusa ace, ndiwo mudzi wopulumukirako wakupha mnzace, ndi Libina ndi mabusa ace;

14. ndi Yatiri ndi mabusa ace, ndi Esitimoa ndi mabusa ace;

15. ndi Holoni ndi mabusa ace, ndi Debiri ndi mabusa ace;

16. ndi Aini ndi mabusa ace, ndi Yuta ndi mabusa ace, ndi Betisemesi ndi mabusa ace; midzi isanu ndi inai yotapira mapfuko awiri aja.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 21