Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 18:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mudzifunire amuna, pfuko liri lonse amuna atatu; kuti ndiwatume, anyamuke, nayendeyende iwo pakati pa dziko, nalilembe monga mwa colowa cao; nabwereoso kwa ine.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 18

Onani Yoswa 18:4 nkhani