Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 17:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo ana a Yosefe ananena ndi Yoswa, ndi kuti, Watipatsiranji colowa cathu camaere cimodzi ndi gawo limodzi, popeza ife ndife anthu aunyinji, pakuti Yehova anatidalitsa ndi pano pomwe?

Werengani mutu wathunthu Yoswa 17

Onani Yoswa 17:14 nkhani