Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 12:9-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. mfumu ya ku Yeriko, imodzi; mfumu ya ku Ai, ndiwo m'mbali mwa Beteli, imodzi;

10. mfumu ya ku Yerusalemu, imodzi; mfumu ya ku Hebroni, imodzi; mfumu ya ku Yarimutu, imodzi;

11. mfumu ya ku Lakisi, imodzi;

12. mfumu ya ku Egiloni, imodzi; mfumu ya ku Gezere, imodzi;

13. mfumu ya ku Dibiri, imodzi; mfumu ya ku Gederi, imodzi;

14. mfumu ya ku Horima, imodzi; mfumu ya ku Haradi, imodzi;

15. mfumu ya ku Libina, imodzi; mfumu ya ku Adulamu, imodzi;

16. mfumu ya ku Makeda, imodzi; mfumu ya ku Beteli, imodzi;

17. mfumu ya ku Tapuwa, imodzi; mfumu ya ku Heferi, imodzi;

18. mfumu ya ku Afeki, imodzi; mfumu ya ku Lasaroni, imodzi;

19. mfumu ya ku Madoni, imodzi; mfumu ya ku Hazori, imodzi;

20. mfumu ya ku Simironi-meroni, imodzi; mfumu ya ku Akasafu, imodzi;

21. mfumu ya ku Taanaki, imodzi; mfumu ya ku Megido, imodzi;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 12