Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 11:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Israyeli, ndipo anawakantha, nawapitikitsa mpaka ku Zidoni waukulu, ndi ku MiseripotuMaimu, ndi ku cigwa ca Mizepe kum'mawa; nawakantha mpaka sanawasiyira ndi mmodzi yense.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 11

Onani Yoswa 11:8 nkhani