Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 11:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kwa Akanani kwn'mawa ndi kumadzulo, ndi kwa Aamori ndi Ahiti, ndi Aperizi ndi Ayebusi kumapiri, ndi kwa Ahivi kunsi kwa Herimoni, m'dziko la Mizipa.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 11

Onani Yoswa 11:3 nkhani