Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 10:42-43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

42. Ndipo Yoswa anagwira mafwnu awa onse ndi dziko lao nthawi yomweyi; cifukwa Yehova Mulungu wa Israyeli anathirira Israyeli nkhondo.

43. Pamenepo Yoswa ndi Aisrayeli onse naye, anabwerera kucigono ku Giligala.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 10