Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 1:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. NDIPO atafa Mose mtumiki wa Yehova, Yehova anati kwa Yoswa mwana wa Nuni mnyamata wa Mose,

2. Mose mtumiki wanga wafa; tauka tsono, nuoloke Yordano uyu, iwe ndi anthu awa onse, kulowa m'dzikomo ndirikuwapatsa, ndiwo ana a Israyeli.

3. Pali ponse phazi lanu lidzapondapo ndinakupatsani, monga ndinanena ndi Mose.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 1