Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yona 1:15-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Momwemo ananyamula Yona, namponya m'nyanja; ndipo nyanja inaleka kukokoma kwace.

16. Ndipo amunawo anaopa Yehova ndi manthaakuru, namphera Yehova nsembe, nawinda.

17. Koma Yehova anaikiratu cinsomba cacikuru cimeze Yona; ndipo Yona anali m'miroba mwa nsombayi masiku atatu usana ndi usiku.

Werengani mutu wathunthu Yona 1