Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 9:28-35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Pamenepo ndiopa zisoni zanga zonse,Ndidziwa kuti simudzandiyesa wosacimwa.

29. Mlandu udzanditsutsa;Potero ndigwire nchito cabe cifukwa ninji?

30. Ndikasamba madzi a cipale cofewaNdi kuyeretsa manja anga ndi sopo;

31. Mudzandibviikanso muli zoola,Ndi zobvala zanga zidzanyansidwa nane.

32. Pakuti sindiye munthu, monga ine, kuti ndimyankhe,Kuti tikomane mlandu.

33. Palibe wakutiweruza,Wakutisanjika ife tonse awiri manja ace.

34. Andicotsere ndodo yace,Coopsa cace cisandicititse mantha;

35. Kuti ndinene, osamuopa,Pakuti sinditero monga umo ndiri.

Werengani mutu wathunthu Yobu 9