14. Anandidzera mantha ndi kunjenjemera,Nanthunthumira nako mafupa anga onse.
15. Pamenepo panapita mzimu pamaso panga;Tsitsi la thupi langa lidati nyau nyau.
16. Unaima ciriri, koma sindinatha kuzindikira maonekedwe ace;Panali mzukwa pamaso panga;Kunali cete, ndipo ndidamva mau akuti,