Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 4:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,

2. Munthu akayesa kunena nawe mau, kodi udzamva nao cisoni?Koma akhoza ndani kudziletsa kunena?

3. Taona iwe walangiza aunyinji,Walimbitsa manja a ofoka.

4. Mau ako anacirikiza iye amene akadagwa,Walimbitsanso maondo otewa.

5. Koma tsopano cakufikira iwe, ndipo ukomoka;Cikukhudza, ndipo ubvutika.

Werengani mutu wathunthu Yobu 4