1. Elihu nabwereza, nati,
2. Mundilole pang'ono, ndidzakuuzani,Pakuti ndiri naonso mau akunenera Mulungu.
3. Ndidzatenga nzeru zanga kutali,Ndidzabvomereza kuti Mlengi wanga ndi wolungama.
4. Pakuti zoonadi, mau anga sali abodza,Wakudziwitsa mwangwiro ali nanu.