Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 34:34-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Anthu ozindikira adzanena nane,Inde anthu anzeru onse akundimva adzati,

35. Yobu alankhula wopanda kudziwa,Ndi mau ace alibe nzeru.

36. Mwenzi nayesedwe Yobu kufikira kutha,Cifukwa ca kuyankha kwace monga anthu amphulupulu,

37. Pakuti pa kucimwa kwace aonjeza kupikisana ndi Mulungu,Asansa manja pakati pa ife,Nacurukitsa maneno ace pa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Yobu 34